Acts 8:37 — Compare Translations
3 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Filipo adayankha kuti, “Mungathe kubatizidwa ngati mukhulupirira ndi mtima wanu wonse.” Iye adati, “Ndikukhulupirira kuti Yesu Khristu ndi Mwana wa Mulungu.”]
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Filipo anati, “Ngati mukhulupirira ndi mtima wanu wonse mukhoza kubatizidwa.” Ndunayo inayankha kuti, “Ine ndikukhulupirira kuti Yesu Khristu ndi Mwana wa Mulungu.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
]