Acts 9:20 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndipo posakhalitsa adayamba kulalika m'nyumba zamapemphero za Ayuda kuti Yesu ndi Mwana wa Mulungu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo pomwepo m'masunagoge analalikira Yesu, kuti Iye ndiye Mwana wa Mulungu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Posakhalitsa anayamba kulalikira mʼsunagoge kuti Yesu ndiye Mwana wa Mulungu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo pomwepo m'masunagoge analalikira Yesu, kuti iye ndiye Mwana wa Mulungu.