Acts 9:23 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Patapita masiku ambiri, Ayuda adapangana kuti aphe Saulo,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo atapita masiku ambiri, Ayuda anapangana kuti amuphe iye;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Patapita masiku ambiri, Ayuda anapangana zoti aphe Saulo,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo atapita masiku ambiri, Ayuda anapangana kuti amuphe iye;