Acts 9:32 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pamene Petro ankayendera anthu a Mulungu uku ndi uku, adakafika kwa amene ankakhala ku Lida.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma kunali, pakupita Petro ponseponse, anatsikiranso kwa oyera mtima akukhala ku Lida.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pamene Petro amayendera mpingo, anapita kukachezera oyera mtima a ku Luda.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma kunali, pakupita Petro ponse ponse, anatsikiranso kwa oyera mtima akukhalaku Luda.