Acts 9:4 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Adagwa pansi namva mau akuti, “Saulo, Saulo, ukundizunziranji Ine?”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ndipo anagwa pansi, namva mau akunena naye, Saulo, Saulo, Undilondalonderanji?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iye anagwa pansi ndipo anamva mawu akuti, “Saulo, Saulo ukundizunziranji Ine?”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
ndipo anagwa pansi, namva mau akunena naye, Saulo, Saulo, Undilondalonderanji?