Amos 1:14 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndiye Ine ndidzaponya moto pa makoma a ku Raba, ndipo motowo udzapsereza malinga ake. Padzakhala kufuula kwakukulu pa tsiku lankhondolo, kumenyana kudzakhala kwafumbi ngati mkuntho wa kamvulumvulu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
koma ndidzayatsa moto pa linga la Raba, udzanyeketsa nyumba zachifumu zake, ndi kufuula tsiku la nkhondo, ndi namondwe, tsiku la kamvulumvulu;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ine ndidzayatsa moto pa makoma a ku Raba umene udzanyeketsa nyumba zake zaufumu. Padzakhala kulira kwakukulu pa tsiku la nkhondoyo, kumenyana kudzakhala kwafumbi ngati mkuntho wa kamvuluvulu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
koma ndidzayatsa moto pa linga la Raba, udzanyeketsa nyumba zacifumu zace, ndi kupfuula tsiku la nkhondo, ndi namondwe, tsiku la kabvumvulu;