Amos 2:10 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Inu Aisraele, ndine ndidakutulutsani ku dziko la Ejipito. Ndine ndidakutsogolerani m'chipululu zaka makumi anai, kuti mukalande dziko la Aamori lija.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo ndinakukwezani kuchokera m'dziko la Ejipito, ndi kukutsogolerani zaka makumi anai m'chipululu, kuti mulandire dziko la Aamori likhale cholowa chanu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Ine ndinakutulutsani ku Igupto, ndipo ndinakutsogolerani mʼchipululu kwa zaka makumi anayi, kudzakupatsani dziko la Aamori.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo ndinakukwezani kucokera m'dziko la Aigupto, ndi kukutsogolerani zaka makumi anai m'cipululu, kuti mulandire dziko la Aamori likhale colowa canu.