Amos 2:12 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Koma Inu mudaŵamwetsa vinyo Anaziri aja, ndipo mudaŵalamula aneneriwo kuti, ‘Musalose.’
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma munamwetsa Anaziri vinyo, ndi kulamulira aneneri ndi kuti, Musamanenera.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Koma inu munawamwetsa vinyo anaziri aja, ndipo munalamula aneneri kuti asanenere.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma munamwetsa Anaziri vinyo, ndi kulamulira aneneri ndi kuti, Musamanenera.