Amos 4:4 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Bwerani ku malo oyera ku Betele, mudzachimwireko. Bweranazoni nsembe zanu m'maŵa mulimonse, bweranazoni zopereka zanu zachikhumi pa masiku atatu aliwonse.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Idzani ku Betele, mudzalakwe ku Giligala, nimuchulukitse zolakwa, nimubwere nazo nsembe zanu zophera m'mawa ndi m'mawa, magawo anu akhumi atapita masiku atatuatatu;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Bwerani ku Beteli mudzachimwe; ndi ku Giligala kuti mudzapitirize kuchimwa. Bweretsani nsembe zanu mmawa uliwonse, bweretsani chakhumi chanu masiku atatu aliwonse.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Idzani ku Beteli, mudzalakwe ku Giligala, nimucurukitse zolakwa, nimubwere nazo nsembe zanu zophera m'mawa ndi m'mawa, magawo anu akhumi atapita masiku atatu atatu;