Amos 7:9 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Akachisi a ana a Isaki adzasanduka bwinja, malo achipembedzo a Aisraele adzaonongedwa. Ndipo ndidzagwetsa banja la mfumu Yerobowamu pa nkhondo.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ndi misanje ya Isaki idzakhala bwinja; ndi malo opatulika a Israele adzapasuka; ndipo ndidzaukira nyumba ya Yerobowamu ndi lupanga.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Malo achipembedzo a Isake adzawonongedwa ndipo malo opatulika a Israeli adzasanduka bwinja; ndidzagwetsa nyumba ya Yeroboamu ndi lupanga langa.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
ndi misanje ya Isake idzakhala bwinja; ndi malo opatulika a Israyeli adzapasuka; ndipo ndidzaukira nyumba ya Yerobiamu ndi lupanga.