Amos 9:2 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Ngakhale akakumbe pansi mpaka ku malo a anthu akufa, dzanja langa lidzaŵadukhululako kumeneko. Ngakhale akakwere mpaka kumwamba, ndidzaŵatsakamutsako.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Angakhale akumba mpaka kunsi kwa manda, dzanja langa lidzawatenga kumeneko; angakhale akwera kumwamba, ndidzawatsitsa komweko.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ngakhale atakumba pansi mpaka ku malo a anthu akufa, dzanja langa lidzawatulutsa kumeneko. Ngakhale atakwera kumwamba Ine ndidzawatsakamutsa kumeneko.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Angakhale akumba mpaka kunsi kwa manda, dzanja langa lidzawatenga kumeneko; angakhale akwera kumwamba, ndidzawatsitsa komweko.