Colossians 2:15 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Motero mwa Khristu Mulungu adaŵalanda zida maufumu ndi maulamuliro onse, ndipo pamaso pa onse, adaŵayendetsa ngati akaidi pa mdipiti wokondwerera kupambana kwake.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
atavula maukulu ndi maulamuliro, anawaonetsera poyera, nawagonjetsera nako.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndipo atalanda zida maufumu ndi maulamuliro, Iye anawachititsa manyazi powayendetsa pamaso pa anthu onse atawagonjetsa ndi mtanda.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
atabvula maukulu ndi maulamuliro, anawaonetsera poyera, nawagonjetsera nako.