Colossians 2:17 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Zonsezi ndi chithunzithunzi chabe cha zinthu zenizeni zimene zilikudza, koma zenizenizo ndi Khristu amene.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ndizo mthunzi wa zilinkudzazo; koma thupi ndi la Khristu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Zimenezi ndi chithunzithunzi chabe cha zinthu zimene zikubwera, koma choonadi chenicheni chikupezeka mwa Khristu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
ndizo mthunzi wa zirinkudzazo; koma thupi ndi la Kristu.