Colossians 2:6 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono popeza kuti mudavomereza kuti Khristu Yesu ndi Mbuye wanu, moyo wanu wonse ukhale wolunzana naye.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Chifukwa chake monga momwe munalandira Khristu Yesu Ambuye, muyende mwa Iye,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tsono popeza munavomereza Khristu Yesu kukhala Ambuye anu, mupitirire kukhala mwa Iyeyo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Cifukwa cace monga momwe munalandira Kristu Yesu Ambuye, muyende mwa iye,