Daniel 1:12 — Compare Translations

3 translations compared side by side

Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Muyesetu anyamata anu masiku khumi; atipatse zomera m'nthaka tidye, ndi madzi timwe.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Chonde mutiyese ife akapolo anu pa masiku khumi: mutipatse masamba okha kuti tidye ndi madzi akumwa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Muyesetu anyamata anu masiku khumi; atipatse zomera m'nthaka tidye, ndi madzi timwe.