Daniel 1:14 — Compare Translations

3 translations compared side by side

Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo anawamvera mau awa, nawayesa masiku khumi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Choncho anawavomera ndipo anawayesa pa masiku khumi.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo anawamvera mau awa, nawayesa masiku khumi.