Daniel 1:15 — Compare Translations

3 translations compared side by side

Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Atatha masiku khumiwo tsono, anaona kuti maonekedwe ao ndi kunenepa kwao anaposa anyamata onse adadyawo zakudya za mfumu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pakutha pa masiku khumi iwo anaoneka athanzi ndi odya bwino kuposa aliyense wa anyamata amene ankadya chakudya cha mfumu aja.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Atatha masiku khumiwo tsono, anaona kuti maonekedwe ao ndi kunenepa kwao anaposa anyamata onse adadyawo zakudya za mfumu.