Daniel 1:18 — Compare Translations
3 translations compared side by side
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Atatha masiku inanenawo mfumu kuti alowe nao, mkulu wa adindo analowa nao pamaso pa Nebukadinezara.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndipo kumapeto kwa masiku amene mfumu inayika kuti adzaonetse anyamatawa ku nyumba yake, mkulu wa nduna za mfumu uja anawapereka iwo kwa Nebukadinezara.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Atatha masiku inanenawo mfumu kuti alowe nao, mkulu wa adindo analowa nao pamaso pa Nebukadinezara.