Daniel 11:33 — Compare Translations
3 translations compared side by side
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo aphunzitsi a anthu adzalangiza ambiri, koma adzagwa ndi lupanga, ndi lawi lamoto, ndi undende, ndi kufunkhidwa masiku ambiri.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Amene ndi anzeru adzalangiza ambiri. Koma patapita kanthawi adzaphedwa ndi lupanga kapena kutenthedwa, kapena kugwidwa kapena kulandidwa katundu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo aphunzitsi a anthu adzalangiza ambiri, koma adzagwa ndi lupanga, ndi lawi lamoto, ndi undende, ndi kufunkhidwa masiku ambiri.