Daniel 11:34 — Compare Translations

3 translations compared side by side

Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo pakugwa iwo adzathandizidwa ndi thandizo laling'ono; koma ambiri adzaphatikizana nao ndi mau osyasyalika.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pa nthawi yozunzikayi ena adzawathandiza pangʼono, koma ambiri othandizawo adzakhala achinyengo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo pakugwa iwo adzathandizidwa ndi thandizo laling'ono; koma ambiri adzaphatikizana nao ndi mau osyasyalika.