Daniel 2:11 — Compare Translations
3 translations compared side by side
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti chinthu achifuna mfumu nchapatali; ndipo palibe wina wokhoza kuchiwulula pamaso pa mfumu, koma milungu imene kwao sikuli pamodzi ndi anthu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Zimene mfumu yafunsa ndi zapatali. Palibe wina amene angathe kuwulula izi kwa mfumu kupatula milungu, ndipo sikhala pakati pa anthu.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti cinthu acifuna mfumu ncapatali; ndipo palibe wina wokhoza kuciulula pamaso pa mfumu, koma milungu imene kwao sikuli pamodzi ndi anthu.