Daniel 2:20 — Compare Translations

3 translations compared side by side

Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Daniele anayankha, nati, Lilemekezedwe dzina la Mulungu kunthawi za nthawi, pakuti nzeru ndi mphamvu zili zake;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
ndipo anati: “Litamandike dzina la Mulungu ku nthawi za nthawi; nzeru ndi mphamvu zonse ndi zake.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Danieli anayankha, nati, Lilemekezedwe dzina la Mulungu ku nthawi za nthawi, a pakuti nzeru ndi mphamvu ziri zace;