Daniel 5:14 — Compare Translations
3 translations compared side by side
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndamva za iwe kuti muli mzimu wa milungu mwa iwe, ndi kuti mupezeka mwa iwe kuunika, ndi luntha, ndi nzeru zopambana.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndamva kuti mzimu wa milungu uli mwa iwe ndi kuti uli ndi chidziwitso, luntha ndi nzeru zapadera.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndamva za iwe kuti muli mzimu wa milungu mwa iwe, ndi kuti mupezeka mwa iwe kuunika, ndi luntha, ndi nzeru zopambana.