Daniel 7:2 — Compare Translations

3 translations compared side by side

Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Daniele ananena, nati, Ndinaona m'masomphenya anga usiku, taonani, mphepo zinai za mumlengalenga zinabuka pa nyanja yaikulu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Danieli anati, “Mʼmasomphenya anga usiku, ndinaona nyanga yayikulu ikuvunduka ndi mphepo zochokera mbali zonse zinayi za mlengalenga.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Danieli ananena, nati, Ndinaona m'masomphenya anga usiku, taonani, mphepo zinai za mumlengalenga zinabuka pa nyanja yaikuru.