Daniel 7:22 — Compare Translations

3 translations compared side by side

Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ndi mlandu unakomera opatulika a Wam'mwambamwamba, nifika nthawi yakuti ufumu unali wao wa opatulikawo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
mpaka pamene Mkulu Wachikhalire uja anafika ndi kuweruza mokomera oyera mtima a Wammwambamwamba. Tsono nthawi inafika imene anthu oyera mtimawo analandira ufumu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
ndi mlandu unakomera opatulika a Wam'mwambamwamba, nifika nthawi yakuti ufumu unali wao wa opatulikawo.