Daniel 8:10 — Compare Translations

3 translations compared side by side

Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Nikula, kufikira khamu la kuthambo; ndi zina za khamulo ndi za nyenyezi inazigwetsa pansi, nizipondereza.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Inakula mpaka inafikira gulu lankhondo la kumwamba, ndipo inagwetsera ena a gulu lankhondolo ndi ena a gulu la nyenyezi ku dziko lapansi ndi kuwapondaponda.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Nikula, kufikira khamu la kuthambo; ndi zina za khamulo ndi za nyenyezi inazigwetsa pansi, nizipondereza.