Daniel 8:14 — Compare Translations
3 translations compared side by side
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Nati kwa ine, Mpaka masiku zikwi ziwiri mphambu mazana atatu usana ndi usiku; pamenepo malo opatulika adzayesedwa olungama.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iye anandiyankha kuti, “Zidzachitika patapita masiku 2,300; pambuyo pake malo opatulika adzabwezeretsedwa monga kale.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Nati kwa ine, Mpaka masiku zikwi ziwiri mphambu mazana atatu usana ndi usiku; pamenepo malo opatulika adzayesedwa olungama.