Deuteronomy 11:8 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Muzimvera zonse zimene ndakulamulani lerozi. Tsono mukatero, mudzakhala amphamvu, ndipo mudzaloŵa ndi kukhazikika m'dzikomo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Potero muzisunga malamulo onsewa ndikuuzani lero lino, kuti mukhale amphamvu, ndi kulowa ndi kulandira dziko, limene mumkako kulilandira;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tsono muzisunga malamulo onse amene ndikukupatsani lero kuti mukhale ndi mphamvu ndi kuti mupite kukalanda mʼdziko limene mwakhala pangʼono kulowamo mukawoloka Yorodani,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Potero muzisunga malamulo onsewa ndikuuzani lero lino, kuti mukhale amphamvu, ndi kulowa ndi kulandira dziko, limene mumkako kulilandira;