Deuteronomy 12:4 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Musakapembedze Chauta, Mulungu wanu, monga m'mene amachitira anthu ameneŵa popembedza milungu yao.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Musamatero ndi Yehova Mulungu wanu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Musapembedze Yehova Mulungu wanu monga mmene amachitira iwowa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Musamatero ndi Yehova Mulungu wanu.