Deuteronomy 13:7 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Milungu yake mwina idzakhala milungu ya anthu omwe mwayandikana nawo, kapena milungu ya amene mwatalikirana nawo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ndiyo milungu ya mitundu ya anthu akuzungulira inu, akukhala pafupi pali inu, kapena akukhala patali pali inu, kuyambira malekezero a dziko lapansi kufikira malekezero ena a dziko lapansi;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
milungu ya anthu okuzungulirani, kaya ndi apafupi kapena akutali, kuchokera kumapeto mpaka kumapeto kwina kwa dziko lapansi),
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
ndiyo milungu ya mitundu ya anthu akuzungulira inu, akukhala pafupi pali inu, kapena akukhala patali pali inu, kuyambira malekezero a dziko lapansi kufikira malekezero ena a dziko lapansi;