Deuteronomy 13:9 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mupheni! Yambani ndinu kumponya miyala, ndipo mutatero, pamenepo aliyense amponyenso miyala.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
koma muzimupha ndithu; liyambe dzanja lanu kukhala pa iye kumupha, ndi pamenepo dzanja la anthu onse.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mumuphe ndithu. Dzanja lanu likhale loyambirira kumupha, kenaka manja a anthu ena onse.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
koma muzimupha ndithu; liyambe dzanja lanu kukhala pa iye kumupha, ndi pamenepo dzanja la anthu onse.