Deuteronomy 14:1 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Inu ndinu anthu a Chauta, Mulungu wanu. Mukamalira maliro, musamadzichekacheka kapena kudzimeta pamphumi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Inu ndinu ana a Yehova Mulungu wanu; musamadzicheka, kapena kumeta tsitsi pakati pa maso chifukwa cha akufa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Inu ndinu ana a Yehova Mulungu wanu. Osamadzichekacheka kapena kudzimeta pamphumi chifukwa cha abale anu amene amwalira,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Inu ndinu ana a Yehova Mulungu wanu; musamadziceka, kapena kumeta tsitsi pakati pa maso cifukwa ca akufa.