Deuteronomy 15:16 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma kapoloyo akakhala kuti akukukondani inu ndi banja lanu, chifukwa mukukhala naye bwino, mwina sangafune nkuchoka komwe. Ngati zili choncho,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo kudzakhala, akanena ndi inu, Sindituluka kuchoka kwanu; popeza akonda inu ndi nyumba yanu, popeza kumkomera kwanu;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma ngati kapoloyo akuwuzani kuti, “Ine sindikufuna kumasulidwa,” chifukwa choti wakukondani inuyo pamodzi ndi banja lanu ndiponso kuti kwamukomera iyeyo kuti azikhalabe nanu,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo kudzakhala, akanena ndi inu, Sindituruka kucoka kwanu; popeza akonda inu ndi nyumba yanu, popeza kumkomera kwanu;