Deuteronomy 17:6 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Munthuyo aphedwe pokhapokha patapezeka mboni ziŵiri kapena zitatu. Asaphedwe chifukwa cha umboni wa munthu mmodzi yekha.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakamwa pa mboni ziwiri kapena zitatu amuphe iye amene akuti afe; asamuphe pakamwa pa mboni imodzi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Munthu aziphedwa pakakhala mboni ziwiri kapena zitatu koma osati mboni imodzi yokha ayi.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakamwa pa mboni ziwiri kapena zitatu amuphe iye amene akuti afe; asamuphe pakamwa pa mboni imodzi.