Deuteronomy 18:11 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pasapezekenso munthu wopempha nzeru kwa mizimu ya anthu akufa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kapena wotsirika, kapena wobwebweta, kapena wopenduza, kapena wofunsira akufa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
wolodza, kapena woyankhula ndi mizimu ya anthu akufa ndi kumafunsira nzeru kwa anthu akufawo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kapena wotsirika, kapena wobwebweta, kapena wopenduza, kapena wofunsira akufa.