Deuteronomy 18:2 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Asakhale ndi choloŵa ngati mafuko ena. Choloŵa chao ndi Chauta amene, potsata malonjezo a Mulungu yemweyo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Alibe cholowa pakati pa abale ao; Yehova mwini wake ndiye cholowa chao, monga ananena nao.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iwowa sadzakhala ndi cholowa pakati pa abale awo pakuti Yehova ndiye cholowa chawo monga anawalonjezera.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Alibe colowa pakati pa abale ao; Yehova mwini wace ndiye colowa cao, monga ananena nao.