Deuteronomy 18:3 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mwa zopereka za anthu, zoyenera kuzilandira ansembeŵa, ndi izi: ng'ombe kapena nkhosa zodzaperekera nsembe, mwendo wamwamba, nyama yam'chibwano ndi chifu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo zoyenera ansembe, awapatse anthu akuphera nsembe ndizo: ingakhale ng'ombe kapena nkhosa azipatsa wansembe mwendo wamwamba, ndi ya m'masaya ndi chifu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Anthu amene abwera kudzapereka nsembe ya ngʼombe kapena nkhosa, azipereka kwa wansembe gawo lake motere: mwendo wakutsogolo, nyama yamʼmasaya ndi zamʼkati.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo zoyenera ansembe, awapatse anthu akuphera nsembe ndizo: ingakhale ng'ombe kapena nkhosa azipatsa wansembe mwendo wamwamba, ndi ya m'masaya ndi chipfu.