Deuteronomy 18:4 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ansembe azilandiranso gawo lanu loyambayamba la tirigu, la vinyo, la mafuta aolivi ndiponso la ubweya.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Zipatso zoyamba za tirigu wanu, za vinyo wanu, ndi za mafuta anu ndi ubweya woyamba kuusenga, muwapatse izi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Muziwapatsa zamasika zoyamba za tirigu wanu, vinyo watsopano ndi mafuta, ndi ubweya woyamba pometa nkhosa zanu,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Zipatso zoyamba za tirigu wanu, za vinyo wanu, ndi za mafuta anu ndi ubweya woyamba kuusenga, muwapatse izi.