Deuteronomy 18:5 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pa mafuko anu onseŵa Chauta adasankhulapo anthu a fuko la Levi ndi ana ao, kuti azigwira ntchito zaunsembe nthaŵi zonse.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Popeza Yehova Mulungu wanu anawasankha mwa mafuko anu onse, aimirire natumikire m'dzina la Yehova, iwo ndi ana ao amuna kosalekeza.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
pakuti Yehova Mulungu wanu wawasankha iwowa ndi ana awo pakati pa mafuko anu onse kuti aziyimirira ndi kutumikira mʼdzina la Yehova nthawi zonse.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Popeza Yehova Mulungu wanu anawasankha mwa mapfuko anu onse, aimirire natumikire m'dzina la Yehova, iwo ndi ana ao amuna kosalekeza.