Deuteronomy 18:7 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndipo kumeneko atumikire Chauta, Mulungu wake, pa unsembe, monga momwe achitira Alevi ena onse amene akutumikira kumeneko.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
pamenepo azitumikira m'dzina la Yehova Mulungu wake, monga amachita abale ake onse Alevi akuimirirako pamaso pa Yehova.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
kumeneko akhoza kukatumikirako mʼdzina la Yehova Mulungu wake monga Alevi anzake onse amene akutumikira pamaso pa Yehova.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
pamenepo azitumikira m'dzina la Yehova Mulungu wace, monga amacita abale ace onse Alevi akuimirirako pamaso pa Yehova.