Deuteronomy 18:8 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ayenera kulandira chakudya molingana ndi ansembe ena, ngakhale ali ndi ndalama chifukwa chogulitsa za m'banja mwake.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Chakudya chao chizifanana, osawerengapo zolowa zake zogulitsa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iye ayenera kulandira zogawana zawo mofanana ndi anzakewo ngakhale kuti iye anagulitsa kale cholowa cha pa banja pawo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Cakudya cao cizifanana, osawerengapo zolowa zace zogulitsa.