Deuteronomy 18:9 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mukadzaloŵa m'dziko limene Chauta, Mulungu wanu, akukupatsanilo, musakatsate machitidwe onyansa a mitundu ya anthu akumeneko.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mutakalowa m'dziko limene Yehova Mulungu wanu akupatsani, musamaphunzira kuchita monga mwa zonyansa za amitundu aja.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mukafika mʼdziko limene Yehova Mulungu wanu akukupatsani, musakaphunzire makhalidwe onyansa a anthu a mʼdzikolo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mutakalowa m'dziko limene Yehova Mulungu wanu akupatsani, musamaphunzira kucita mongamwa zonyansa za amitundu aja.