Deuteronomy 19:17 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
aŵiri onsewo abwere, adzaimirire pamaso pa Chauta. Kumeneko aŵaweruze ansembe ndi aweruzi amene ali pa ntchito nthaŵi imeneyo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
pamenepo anthu onse awiri, pakati pao pali makaniwo, aziima pamaso pa Yehova, pamaso pa ansembe ndi oweruza okhala m'masiku awa;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
anthu awiri okhudzidwa ndi mlanduwo ayenera kuyima pamaso pa Yehova pali ansembe ndi oweruza amene ali pa ntchito pa nthawiyo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
pamenepo anthu onse awiri, pakati pao pali makaniwo, aziima pamaso pa Yehova, pamaso pa ansembe ndi oweruza okhala m'masiku awa;