Deuteronomy 19:8 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chauta, Mulungu wanu, akadzakuza dziko lanu monga momwe adalonjezera makolo anu, ndipo akadzakupatsani dziko lonse limene adalonjeza,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Yehova Mulungu wanu akakulitsa malire anu, monga analumbirira makolo anu, ndi kukupatsani dziko lonse limene ananena kwa makolo anu kuwapatsa ili;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ngati Yehova Mulungu wanu akulitsa malire anu monga analonjezera pa malumbiro ndi makolo anu, nakupatsani dziko lonse monga analonjezera,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Yehova Mulungu wanu akakulitsa malire anu, monga analumbirira makolo anu, ndi kukupatsani dziko lonse limene ananena kwa makolo anu kuwapatsa ili;