Deuteronomy 20:17 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Muŵaononge kotheratu onse anthu aŵa: Ahiti, Aamori, Akanani, Aperizi, Ahivi ndi Ayebusi, monga momwe Chauta Mulungu wanu adakulamulirani.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
koma muwaononge konse Ahiti, ndi Aamori, Akanani, ndi Aperizi, Ahivi ndi Ayebusi; monga Yehova Mulungu wanu anakulamulirani;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Muwawononge kwathunthu Ahiti, Aamori, Akanaani, Aperezi, Ahivi ndi Ayebusi monga momwe Yehova Mulungu wanu anakulamulirani.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
koma muwaononge konse Ahiti, ndi Aamori, Akanani, ndi Aperizi, Ahivi ndi Ayebusi; monga Yehova Mulungu wanu anakulamulirani;