Deuteronomy 20:2 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Musanayambe kumenya nkhondo, wansembe abwere, ndipo auze ankhondowo kuti,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo kudzali, pamene muyandikiza kunkhondo, ayandikize wansembe nanene ndi anthu,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pamene mwatsala pangʼono kuyamba nkhondo, wansembe azibwera kutsogolo ndipo aziyankhula ku gulu lonse lankhondolo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo kudzali, pamene muyandikiza kunkhondo, ayandikize wansembe nanene ndi anthu,