Deuteronomy 20:5 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pamenepo akuluakulu a ankhondo adzauza anthu kuti, “Kodi alipo pano munthu amene wangomanga nyumba yatsopano, koma sanaipereke kwa Mulungu? Ngati alipo abwerere kwao, mwinamwina akaphedwa pa nkhondo, ndiye kuti ndi wina amene adzaipereka nyumbayo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo akapitao anene ndi anthu, ndi kuti, Ndani munthuyo anamanga nyumba yatsopano, osalowamo? Amuke nabwerere kunyumba kwake, kuti angafe kunkhondo nangalowemo munthu wina.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Akuluakulu ankhondo adzati kwa gulu la ankhondolo, “Kodi pali wina amene wangomanga nyumba kumene ndipo sanayitsekulire? Ayambe wapita ku mudzi chifukwa mwina akafera ku nkhondoko ndipo wina ndi kudzayitsekulira.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo akapitao anene ndi anthu, ndi kuti, Ndani munthuyo anamanga nyumba yatsopano, osalowamo? amuke nabwerere kunyumba kwace, kuti angafe kunkhondo nangalowemo munthu wina.