Deuteronomy 21:15 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tiyese kuti munthu ali ndi akazi aŵiri, wina wokondedwa kwambiri wina pang'ono, onsewo nkubala ana aamuna, mwana woyamba kubadwa nakhala wa mkazi amene amamkonda pang'ono.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Munthu akakhala nao akazi awiri, wina wokondana naye, wina wodana naye, nakambalira ana, wokondana naye, ndi wodana naye yemwe; ndipo mwana wamwamuna woyamba akakhala wa iye uja anadana naye;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ngati munthu ali ndi akazi awiri, nakonda wina koposa mnzake, onsewa ndikubereka ana aamuna koma woyamba nakhala mwana wa mkazi amene samukondayo,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Munthu akakhala nao akazi awiri, wina wokondana naye, wina wodana naye, nakambalira ana, wokondana naye, ndi wodana naye yemwe; ndipo mwana wamwamuna woyamba akakhala wa iye uja anadana naye;