Deuteronomy 22:13 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mwina munthu angathe kukwatira mtsikana, namakhala naye ndithu, pambuyo pake nkunena kuti mkaziyo sakumfuna.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Munthu akatenga mkazi, nalowana naye, namuda,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ngati munthu akwatira mkazi, ndipo atagona naye nʼkusamufunanso
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Munthu akatenga mkazi, nalowana naye, namuda,