Deuteronomy 22:25 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mwina munthu, kuthengo koteroko, achita kugwirira mtsikana wofunsidwa mbeta nachita naye chigololo momkakamiza. Zikatero, munthu wamwamuna yekhayo ndiye aphedwe.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma mwamuna akapeza namwali wopalidwa bwenzi kuthengo, namgwira mwamunayo, nagona naye; pamenepo afe mwamuna yekha wogona naye;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma ngati munthu akumana ndi mkazi kutchire yemwe anachita kale chinkhoswe namugwiririra, mwamuna yekhayo ndiye woyenera kuphedwa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma mwamuna akapeza namwali wopalidwa bwenzi kuthengo, namgwira mwamunayo, nagona naye; pamenepo afe mwamuna yekha wogona naye;